July 10-16
EZARA 7-8
Nyimbo Na. 82 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (1 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Zochita za Ezara Zinachititsa Kuti Dzina la Yehova Lilemekezedwe”: (10 min.)
Mfundo Zothandiza: (10 min.)
Eza 8:1—N’chifukwa chiyani Ayuda ambiri ku Babulo ananyalanyaza kupita ku Yerusalemu ndi Ezara? (w06 1/15 19 ¶10)
Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?
Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Eza 8:21-36 (th phunziro 5)
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Vidiyo ya Ulendo Wobwereza: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo ya Ulendo Wobwereza: Kuvutika—1Yo 5:19. Muziimitsa vidiyoyi nthawi iliyonse imene pali chizindikiro chosonyeza kuti muime n’kufunsa omvera mafunso omwe ali muvidiyoyi.
Ulendo Wobwereza: (3 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo wobwereza. Yerekezerani kumuonetsa vidiyo yakuti N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuphunzira Baibulo? kenako kambiranani naye mfundo za muvidiyoyi (th phunziro 4)
Ulendo Wobwereza: (5 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo wobwereza. Mugawireni kabuku kakuti Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, ndipo musonyezeni mmene phunziro la Baibulo limachitikira. (th phunziro 11)
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Zofunika Pampingo: (15 min.)
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lff phunziro 50 mfundo 1-5 komanso vidiyo yakuti Tetezani Ana Anu yomwe ili mu kabokosi kakuti “Kodi Mukudziwa?”
Mawu Omaliza (3 min.)
Nyimbo Na. 134 ndi Pemphero