Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

July 24-30

NEHEMIYA 1-2

July 24-30

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Nthawi Yomweyo Ndinapemphera”: (10 min.)

  • Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Ne 2:4​—Kodi aka kanali koyamba kuti Nehemiya apemphere zokhudza nkhaniyi, nanga tikuphunzirapo chiyani? (w86 2/15 25)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Ne 2:11-20 (th phunziro 2)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 44

  • Khalani Bwenzi la Yehova​—Kodi Yehova Amayankha Mapemphero?: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako funsani omvera kuti, Kodi vidiyoyi ikutiphunzitsa chiyani zokhudza pemphero?

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lff phunziro 51

  • Mawu Omaliza (3 min.)

  • Nyimbo Na. 102 ndi Pemphero