July 24-30
NEHEMIYA 1-2
Nyimbo Na. 47 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (1 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Nthawi Yomweyo Ndinapemphera”: (10 min.)
Mfundo Zothandiza: (10 min.)
Ne 2:4—Kodi aka kanali koyamba kuti Nehemiya apemphere zokhudza nkhaniyi, nanga tikuphunzirapo chiyani? (w86 2/15 25)
Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?
Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Ne 2:11-20 (th phunziro 2)
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Ulendo Woyamba: (3 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo woyamba. Kenako mufotokozereni za webusaiti yathu ya jw.org, ndipo mugawireni khadi lodziwitsa anthu za webusaitiyi. (th phunziro 16)
Ulendo Wobwereza: (4 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo wobwereza. Mugawireni chimodzi mwa Zinthu Zophunzitsira. (th phunziro 3)
Phunziro la Baibulo: (5 min.) lff phunziro 11 mawu oyamba pa mbali yakuti Fufuzani Mozama komanso mfundo 4 (th phunziro 11)
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Khalani Bwenzi la Yehova—Kodi Yehova Amayankha Mapemphero?: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako funsani omvera kuti, Kodi vidiyoyi ikutiphunzitsa chiyani zokhudza pemphero?
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lff phunziro 51
Mawu Omaliza (3 min.)
Nyimbo Na. 102 ndi Pemphero