CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Kodi Mumagwira Ntchito Zonyozeka?
Mkulu wa ansembe ndi abale ake sanadzione kukhala anthu apamwamba kwambiri ndipo anagwira nawo ntchito yomanganso mpanda wa Yerusalemu (Ne 3:1)
Anthu ena otchuka “sanagonjere” kuti agwire nawo ntchitoyo (Ne 3:5; w06 2/1 10 ¶1)
Akazi okhulupirika anagwira nawo ntchitoyi yomwe inali yovuta komanso yofuna mphamvu zambiri (Ne 3:12; w19.10 23 ¶11)
Ntchito zambiri zimene zimachitika pampingo, zimafuna mphamvu kapena zimakhala zonyozeka komanso zina ena sangatione tikuzigwira.—w04 8/1 18 ¶16.
DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndimamva bwanji ndikamagwira ntchito zoterezi, zomwe zimathandiza pa ntchito ya uthenga wabwino?’—1Ak 9:23.