August 12-18
MASALIMO 73-74
Nyimbo Na. 36 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)
1. Kodi Ndimachitira Nsanje Anthu Amene Satumikira Mulungu?
(10 min.)
Tikhoza kuyamba kuchitira nsanje anthu amene satumikira Yehova (Sl 73:3-5; w20.12 19 ¶14)
Tikamalambira Yehova limodzi ndi abale ndi alongo athu m’malo modzipatula, tikhoza kuyamba kuwaona bwino anthu amene satumikira Mulungu (Sl 73:17; Miy 18:1; w20.12 19 ¶15-16)
Anthu omwe satumikira Mulungu ali “pamalo oterera”; pomwe amene amamutumikira amawapatsa “ulemerero” (Sl 73:18, 19, 24; w14 4/15 4 ¶5; w13 2/15 25-26 ¶3-5)
2. Mfundo Zothandiza
(10 min.)
Sl 74:13, 14—Kodi mawu akuti “Leviyatani” amanena za chiyani? (it-2 240)
Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
3. Kuwerenga Baibulo
(4 min.) Sl 74:1-23 (th phunziro 10)
4. Ulendo Woyamba
(3 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Pezani mwayi woti muuze mnzanu zimene mwaphunzira pa misonkhano yampingo yaposachedwapa. (lmd phunziro 2 mfundo 4)
5. Ulendo Wobwereza
(4 min.) KULALIKIRA M’MALO OPEZEKA ANTHU AMBIRI. M’pempheni kuti muziphunzira naye Baibulo ndipo musonyezeni mmene phunziro limachitikira. (lmd phunziro 8 mfundo 3)
6. Kufotokoza Zimene Mumakhulupirira
(5 min.) Nkhani. ijwbq 89—Mutu: Kodi Zipembedzo Zonse N’zabwino? (th phunziro 14)
Nyimbo Na. 72
7. Zofunika Pampingo
(15 min.)
8. Phunziro la Baibulo la Mpingo
(30 min.) bt mutu 14 ¶1-6, bokosi patsamba 112