Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

March 14-20

YOBU 1-5

March 14-20
  • Nyimbo Na. 89 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 88

  • Musamangotengera Zochita za Anzanu: (15 min.) Nkhani yokambirana. Yambani ndi kuonetsa vidiyo ya pa jw.org yakuti Musamangotengera Zochita za Anzanu (Pitani pamene palembedwa kuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ACHINYAMATA.) Kenako funsani mafunso otsatirawa: Kodi ana amakumana ndi mavuto otani kusukulu? Kodi angagwiritse ntchito bwanji mfundo ya pa Ekisodo 23:2? Kodi ndi zinthu 4 ziti zimene zingawathandize kuti asamangotengera zochita za anzawo komanso kuti akhalebe okhulupirika kwa Mulungu? Pemphani achinyamata kuti afotokoze zinthu zabwino zimene anakumana nazo kusukulu.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: cl mutu 27 ndime 10-18 (30 min.)

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 149 ndi Pemphero