Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

March 21-27

YOBU 6-10

March 21-27
  • Nyimbo Na. 68 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: wp16.2 16—Muuzeni munthu amene mukumulalikirayo kuti angathe kupereka ndalama zothandizira ntchito yathu yapadziko lonse. (Osapitirira 2 min.)

  • Ulendo Wobwereza: wp16.2 16—Muuzeni nkhani imene mudzaphunzire ulendo wotsatira. (Osapitirira 4 min.)

  • Phunziro la Baibulo: fg phunziro 2 ndime 6-8 (Osapitirira 6 min.)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 114

  • Muzichita Zinthu Mozindikira Mukamalimbikitsa Ena: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onetsani vidiyo imene akulu anaonera pa Sukulu ya Utumiki wa Ufumu yomwe inachitika posachedwapa. Kenako pemphani omvera kuti afotokoze mmene abale awiri a m’vidiyoyi asonyezera chitsanzo chabwino polimbikitsa munthu amene wakhumudwa chifukwa cha imfa ya munthu amene amam’konda.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: cl mutu 27 ndime 19-22 ndi bokosi patsamba 279 (30 min.)

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 27 ndi Pemphero