March 28–April 3
YOBU 11-15
Nyimbo Na. 111 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Yobu Sankakayikira Kuti Akufa Adzauka”: (10 min.)
Yobu 14:1, 2—Yobu ananena zinthu zimene zimasonyeza mmene moyo wa anthu ulili masiku ano (w15 3/1 3; w10 5/1 5 ndime 2; w08 3/1 3 ndime 3)
Yobu 14:13-15a—Yobu ankadziwa kuti Yehova sangamuiwale (w15 8/1 5; w14 1/1 7 ndime 4; w11 3/1 22 ndime 2-4)
Yobu 14:15b—Yehova amaona kuti atumiki ake okhulupirika ndi ofunika kwambiri (w15 8/1 7 ndime 3; w14 6/15 14 ndime 12; w11 3/1 22 ndime 3-6)
Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)
Yobu 12:12—N’chifukwa chiyani tinganene kuti Akhristu achikulire angathandize Akhristu achinyamata? (g99 8/8 11, bokosi)
Yobu 15:27—Kodi Elifazi ankatanthauza chiyani pamene ananena kuti nkhope ya Yobu “yaphimbika ndi mafuta”? (it-1-E 802 ndime 4)
Kodi ndaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kodi ndi mfundo ziti zimene ndaphunzira mlungu uno zimene ndingazigwiritse ntchito mu utumiki?
Kuwerenga Baibulo: Yobu 14:1-22 (Osapitirira 4 min.)
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Ulendo Woyamba: fg phunziro 13, ndime 1—Muuzeni zimene mudzakambirane mukadzabweranso. (Osapitirira 2 min.)
Ulendo Wobwereza: fg phunziro 13, ndime 2—Kenako amuuze zimene adzaphunzire akadzabweranso. (Osapitirira 4 min.)
Phunziro la Baibulo: fg phunziro 13, ndime 3-4 (Osapitirira 6 min.)
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Nyimbo Na. 134
Zofunika pampingo: (5 min.)
“Imfa ya Yesu Inathandiza Kuti Akufa Adzaukitsidwe”: (10 min.) Nkhani yokambirana. Pomaliza onetsani vidiyo imene inaonetsedwa pa Msonkhano Wachigawo wa 2014 wakuti, “Pitirizani Kufunafuna Ufumu wa Mulungu Choyamba.”
Phunziro la Baibulo la Mpingo: cl mutu 28 ndime 1-9 (30 min.)
Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)
Nyimbo Na. 33 ndi Pemphero