Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

March 6-12

YEREMIYA 1-4

March 6-12
  • Nyimbo Na. 23 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Kukonzekera Ulaliki wa Mwezi Uno: (15 min.) Kukambirana Zitsanzo za Ulaliki. Pambuyo poonetsa vidiyo ya chitsanzo cha ulaliki iliyonse, kambiranani mfundo zikuluzikulu za m’vidiyoyo.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 149

  • Zimene Gulu Lathu Lachita: (7 min.) Onetsani vidiyo ya Zimene Gulu Lathu Lachita ya March.

  • Ntchito Yoitanira Anthu ku Chikumbutso Idzayamba pa 18 March: (8 min.) Nkhani yokambidwa ndi woyang’anira utumiki yochokera mu Ndandanda ya Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu ya February 2016, tsamba 8. Perekani kapepala koitanira anthu ku Chikumbutso kwa aliyense n’kukambirana mfundo zake. Fotokozani zimene mpingo wakonza pofuna kuti mudzathe kugawira timapepalati kwa anthu onse a m’gawo lanu.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia mutu 19 ¶1-16

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 74 ndi Pemphero