Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YEREMIYA 1-4

“Ine Ndili ndi Iwe Kuti Ndikulanditse”

“Ine Ndili ndi Iwe Kuti Ndikulanditse”

N’kutheka kuti Yeremiya anali ndi zaka pafupifupi 25 pamene Yehova anamuika kukhala mneneri. Yeremiya ankaona kuti sangakwanitse ntchito imeneyi, koma Yehova anamutsimikizira kuti amuthandiza.

  1. 647

    Yeremiya anaikidwa kukhala mneneri

  2. 607

    Yerusalemu anawonongedwa

  3. 580

    Nthawi imene anamaliza kulemba bukuli

Zaka zonsezi ndi za B.C.E.