March 5-11
Mateyu 20-21
Nyimbo Na. 76 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Aliyense Wofuna Kukhala Wamkulu Pakati Panu Ayenera Kukhala Mtumiki Wanu”: (10 min.)
Mat. 20:3—Alembi ndi Afarisi onyada ankasangalala akamalemekezedwa komanso kupatsidwa ulemu “pamsika” (Zithunzi ndi mavidiyo za “pamsika” pa Mat. 20:3, nwtsty)
Mat. 20:20, 21—Atumwi awiri anapempha kuti apatsidwe udindo komanso malo aulemu (Mfundo zimene ndikuphunzira za “mkazi wa Zebedayo,” “mmodzi kudzanja lanu lamanja, wina kumanzere kwanu” pa Mat. 20:20, 21, nwtsty)
Mat. 20:25-28—Yesu anafotokoza kuti otsatira ake ayenera kukhala odzichepetsa (Mfundo zimene ndikuphunzira za “mtumiki” pa Mat. 20:26, nwtsty)
Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)
Mat. 21:9—Kodi anthu amene ankafuula kuti, “M’pulumutseni Mwana wa Davide!” ankatanthauza chiyani? (Mfundo zimene ndikuphunzira za “M’pulumutseni,” “Mwana wa Davide” pa Mat. 21:9, nwtsty)
Mat. 21:18, 19—Kodi n’chifukwa chiyani Yesu anachititsa kuti mtengo wa mkuyu ufote? (jy 244 ¶4-6)
Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Mat. 20:1-19
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.
Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha zimene tinganene.
Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) lv 36-37 ¶3-4
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Zofunika Pampingo: (5 min.)
Zimene Gulu Lathu Lachita: (10 min.) Onetsani vidiyo ya Zimene Gulu Lathu Lachita ya March.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 15 ¶1-8
Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)
Nyimbo Na. 53 ndi Pemphero