Pitirizani Kukhala Maso M’masiku Otsiriza Ano
Anthu ambiri masiku ano amalola kuti zinthu zatsiku ndi tsiku ziwalepheretse kuchita zinthu zokhudza kulambira. Kodi Akhristu olimba mwauzimu amasiyana bwanji ndi anthu a m’dzikoli pa nkhani ya mmene amaonera . . .
-
maphunziro apamwamba?
-
zosangalatsa?
-
ntchito?
-
chuma?