NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU March 2020
Zimene Tinganene
Zitsanzo za zimene tinganene zokhudza Yesu Khristu komanso nsembe imene anapereka.
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
‘Mulungu Anayesa Abulahamu’
Kodi n’chifukwa chiyani Yehova anauza Abulahamu kuti apereke mwana wake ngati nsembe?
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Isaki Anapeza Mkazi
Kodi tingaphunzire chiyani kwa mtumiki wa Abulahamu tikafuna kusankha zochita pa nkhani zikuluzikulu?
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Kodi Ndiitane Ndani?
Kodi mukufuna kudzaitana ndani pa mwambo wokumbukira imfa ya Khristu umene ukubwera kutsogoloku?
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Esau Anagulitsa Ukulu Wake
Kodi ndi zinthu zopatulika ziti zomwe muyenera kuyamikira?
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Yakobo Analandira Madalitso
Kodi Yakobo analandira bwanji madalitso ake?
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Yakobo Anakwatira
Kodi mungatani kuti muzikhalabe osangalala m’banja ngakhale mutakumana ndi mavuto?
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Muzilalikira Anthu Osaona
Kodi tingatengere bwanji chitsanzo cha Yehova tikamathandiza anthu osaona m’gawo lathu?