Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

March 16-22

GENESIS 25-26

March 16-22

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Esau Anagulitsa Ukulu Wake”: (10 min.)

    • Ge 25:27, 28​—Esau ndi Yakobo anali ana amapasa koma anali ndi makhalidwe osiyana komanso ankakonda zosiyana (it-1 1242)

    • Ge 25:29, 30​—Esau anachita zinthu mosaganiza bwino chifukwa cha njala komanso kutopa

    • Ge 25:31-34​—Esau anagulitsa ukulu wake pousinthanitsa ndi chakudya chifukwa sankayamikira zinthu zopatulika (w19.02 16 ¶11; it-1 835)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Ge 25:31-34​—Kodi nkhaniyi ikusonyeza bwanji kuti si nthawi zonse pamene mwana woyamba kubadwa ankakhala mumzere wa makolo a Mesiya? (Ahe 12:16; w17.12 15 ¶5-7)

    • Ge 26:7​—N’chifukwa chiyani Isaki sananene zoona pa nthawi imeneyi? (it-2 245 ¶6)

    • Kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ge 26:1-18 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

MOYO WATHU WACHIKHRISTU