Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

March 2-8

GENESIS 22-23

March 2-8

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Mulungu Anayesa Abulahamu”: (10 min.)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Ge 22:5​—N’chifukwa chiyani Abulahamu anatsimikizira antchito ake kuti Isaki abweranso, pomwe ankadziwa kuti akukamupereka nsembe? (w16.02 11 ¶13)

    • Ge 22:12​—Kodi lembali likusonyeza bwanji kuti Yehova amachita kusankha zinthu zoti adziwiretu? (it-1 853 ¶5-6)

    • Kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ge 22:1-18 (th phunziro 2)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 4

  • Kumvera Kunawateteza: (15 min.) Onerani vidiyo yakuti Msonkhano Wapachaka wa 2017​—Nkhani Komanso Lemba la Chaka cha 2018​—Mbali ina ya vidiyoyi.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 75

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (Osapitirira 3 min.)

  • Nyimbo Na. 111 ndi Pemphero