Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

March 30–April 5

GENESIS 29-30

March 30–April 5

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Yakobo Anakwatira”: (10 min.)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Ge 30:3​—N’chifukwa chiyani Rakele ankaona ana amene Yakobo anabereka ndi Biliha ngati ake? (it-1 50)

    • Ge 30:14, 15​—N’chifukwa chiyani Rakele anataya mwayi wake woti akanatha kutenga pakati pousinthanitsa ndi mandereki? (w04 1/15 28 ¶7)

    • Kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ge 30:1-21 (th phunziro 2)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 57

  • Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki​—Muzilalikira Anthu Osaona”: (10 min.) Nkhani yokambidwa ndi woyang’anira utumiki. Funsani omvetsera mafunso otsatirawa: N’chifukwa chiyani tiyenera kuyesetsa kuti tizilalikira anthu osaona? Kodi anthu osaona tingawapeze bwanji? Kodi tingasonyeze bwanji kuti timawaganizira tikamawalalikira? Kodi tili ndi zinthu ziti zomwe zingawathandize kuti akhale pa ubwenzi ndi Yehova?

  • Zimene Gulu Lathu Lachita: (5 min.) Onerani vidiyo ya Zimene Gulu Lathu Lachita ya March.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 79

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (Osapitirira 3 min.)

  • Nyimbo Na. 127 ndi Pemphero