CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Yehova Amasintha Temberero N’kukhala Dalitso
Amowabu ankafuna kuchitira zoipa Aisiraeli (Nu 22:3-6)
Yehova anathandiza anthu ake (Nu 22:12, 34, 35; 23:11, 12)
Palibe amene angalimbane ndi Yehova (Nu 24:12, 13; bt 53 ¶5; it-2 291)
Vuto lililonse, ngakhalenso chizunzo, silingalepheretse kuti uthenga wabwino ulalikidwe mogwirizana ndi chifuniro cha Mulungu. Tikakumana ndi mavuto, kodi timadalira Atate wathu wakumwamba n’kumaonabe kuti kumulambira ndiye kofunika kwambiri?