CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Ine Ndine . . . Cholowa Chako”
Yehova anapatsa ansembe ndi Alevi mwayi wapadera wochita utumiki wofunika kwambiri (Nu 18:6, 7)
Anthu a fuko la Levi sanalandire cholowa cha malo. Cholowa chawo anali Yehova (Nu 18:20, 24; w11 9/15 13 ¶9)
Aisiraeli ankapereka chakhumi pa zokolola zawo kuti chizithandiza Alevi ndi ansembe (Nu 18:21, 26, 27; w11 9/15 7 ¶4)
Yehova analonjeza Alevi ndi ansembe kuti aziwapatsa zofunika pa moyo. Sitiyenera kukayikira kuti Yehova adzatisamalira ngati titadzimana zinthu zina n’cholinga choti tizimutumikira.