CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Mmene Chikhulupiriro Chimatithandizira Kukhala Olimba Mtima
Azondi amene anapereka lipoti labodza analibe chikhulupiriro (Nu 13:31-33; 14:11)
Kupanda chikhulupiriro kwa azondi 10 kunafooketsa abale awo (Nu 14:1-4)
Azondi amene anapitiriza kukhala olimba mtima anali ndi chikhulupiriro cholimba (Nu 14:6-9; w06 10/1 17 ¶5-6)
Aisiraeli anali ataona kale mmene Yehova anawapulumutsira m’mbuyomo. Zimenezi zinkayenera kulimbitsa chikhulupiriro chawo kuti awathandiza kugonjetsa Akanani.