Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

March 8-14

NUMERI 9–10

March 8-14

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Yehova Amatsogolera Anthu Ake”: (10 min.)

  • Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Nu 9:13​—Kodi tikuphunzira chiyani pa malangizo amene Aisiraeli anapatsidwawa? (it-1 199 ¶3)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Nu 10:17-36 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 84

  • Kusintha Zinthu pa Beteli Kukuthandiza pa Ntchito Yolalikira: (10 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: Kodi pamsonkhano wapachaka wa 2015 panaperekedwa chilengezo chotani, nanga ndi zifukwa ziwiri ziti zomwe zinachititsa kuti pakhale kusintha? Kodi ndi zinthu zina ziti zimene zinasintha pa Beteli, ndipo kusinthaku kwathandiza bwanji? Kodi chilengezochi chinakhudza bwanji ntchito yosamutsa nthambi ya ku Britain? Kodi kusintha kumeneku kukusonyeza bwanji kuti Yehova akutitsogolera?

  • Chimene Tinabwerera ku Beteli: (5 min.) Onerani vidiyoyi.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 124

  • Mawu Omaliza (3 min.)

  • Nyimbo Na. 113 ndi Pemphero