April 10-16
2 Mbiri 8-9
Nyimbo Na. 88 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (1 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Mfumukazi Inaona Kuti Nzeru Ndi Zamtengo Wapatali”: (10 min.)
Mfundo Zothandiza: (10 min.)
2Mb 9:19—Kodi n’kutheka kuti zifaniziro 12 za mikango zomwe zinali pa masitepe okafika kumpando wachifumu wa Solomo zinkaimira chiyani? (it-2 1097)
Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?
Kuwerenga Baibulo: (4 min.) 2Mb 8:1-16 (th phunziro 5)
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo ya Ulendo Woyamba: Yesu—Mt 16:16. Muziimitsa vidiyoyi nthawi iliyonse imene pali chizindikiro chosonyeza kuti muime n’kufunsa omvera mafunso omwe ali muvidiyoyi.
Ulendo Woyamba: (3 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo woyamba. Sonyezani mmene mungayankhire munthu amene wanena zinthu zina zomwe anthu amakonda kunena ngati sakufuna kuti tikambirane nawo. (th phunziro 2)
Phunziro la Baibulo: (5 min.) lff phunziro 09 mfundo 6 (th phunziro 19)
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
“Muziwerenga Baibulo Tsiku Lililonse Komanso Muzifunafuna Nzeru”: (15 min.) Nkhani yokambirana komanso vidiyo.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lff phunziro 42 ndi mawu akumapeto 4
Mawu Omaliza (3 min.)
Nyimbo Na. 131 ndi Pemphero