CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Mfumukazi Inaona Kuti Nzeru Ndi Zamtengo Wapatali
Mfumukazi ya ku Sheba inayenda ulendo wautali komanso wovuta kuti ikaone Solomo (2Mb 9:1, 2; w99 11/1 20 ¶4; w99 7/1 30 ¶4-5)
Nzeru komanso chuma cha Solomo zinamusowetsa chonena (2Mb 9:3, 4; w99 7/1 30-31; onani chithunzi chapachikuto)
Zimene anaona zinamuchititsa kuti atamande Yehova (2Mb 9:7, 8; it-2 990-991)
Mfumukazi ya ku Sheba inaona kuti nzeru ndi zamtengo wapatali moti inachita zonse zomwe ikanatha kuti ikhale nazo.
DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndine wofunitsitsa kufunafuna nzeru ngati mmene ndingachitire ndi chuma chobisika?’—Miy 2:1-6.