CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Thawirani kwa Yehova
Mu Isiraeli munali mizinda 6 yoti amene wapha munthu mwangozi azithawirako (Nu 35:15; w17.11 9 ¶4)
Akulu a mu Isiraeli ankaweruza mlandu uliwonse (Nu 35:24; w17.11 9 ¶6)
Mizinda yothawirako inali malo achitetezo (Nu 35:25; w17.11 11 ¶13)
Mofanana ndi munthu yemwe wapha mnzake mwangozi amene ankafunika kusiya moyo umene anazolowera kuti akhale ndi mwayi wotetezedwa ndi mizinda yothawirako, ifenso timafunika kusiya zinthu zina kuti Yehova atichitire chifundo n’kutikhululukira.