May 3-9
NUMERI 27-29
Nyimbo Na. 106 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (1 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Muzitsanzira Yehova Yemwe Ndi Wosakondera”: (10 min.)
Mfundo Zothandiza: (10 min.)
Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Nu 28:11-31 (th phunziro 5)
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Ulendo Woyamba: Cholinga cha Mulungu—Ge 1:28. Muziimitsa nthawi iliyonse imene pali chizindikiro chosonyeza kuti muime n’kufunsa omvera mafunso omwe ali m’vidiyoyi.
Ulendo Woyamba: (3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. (th phunziro 4)
Nkhani: (5 min.) w07 4/1 17-18—Mutu: Kodi N’chiyani Chimachititsa Kuti Yehova Azisangalala Ndi Nsembe Zathu? (th phunziro 16)
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Nyimbo Na. 82
Khalani Bwenzi la Yehova—Uzikonda Mnzako: (6 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako ngati n’zotheka, funsani ana omwe munawasankhiratu mafunso awa: N’chifukwa chiyani ana ena sankafuna kuchita zinthu ndi Priya kusukulu? Kodi Sofiya anasonyeza bwanji chikondi kwa Priya? Kodi mungasonyeze bwanji chikondi kwa anthu omwe ndi osiyana ndi inu?
Kodi Mnzako Weniweni Ungamudziwe Bwanji?: (9 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yamakatuniyi. Kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: Kodi muyenera kuyang’ana zinthu ziti mukamasankha anzanu? Kodi anzanu abwino mungawapeze kuti? Kodi mungatani kuti ubwenzi wanu uziyenda bwino?
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 132 ndi bokosi lakuti “Mpachikeni”
Mawu Omaliza (3 min.)
Nyimbo Na. 20 ndi Pemphero