Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

Zimene Tinganene

Zimene Tinganene

Ulendo Woyamba

Funso: Kodi Mulungu analenga anthu chifukwa chiyani?

Lemba: Ge 1:28

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi timadziwa bwanji kuti cholinga cha Mulungu polenga anthu chidzakwaniritsidwa?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

Ulendo Wobwereza

Funso: Kodi timadziwa bwanji kuti cholinga cha Mulungu polenga anthu chidzakwaniritsidwa?

Lemba: Yes 55:11

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi moyo udzakhala wotani Mulungu akadzakwaniritsa cholinga chimene analengera anthu?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU: