CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Kudzikonda kwa Aminoni Kunabweretsa Mavuto
Aminoni anatengeka ndi Tamara (2Sa 13:1, 2; it-1 32)
Aminoni anagwiririra Tamara (2Sa 13:10-15; w17.09 5 ¶11)
Abisalomu anachititsa kuti Aminoni aphedwe (2Sa 13:28, 29; it-1 33 ¶1)
Kodi amene ali pachibwenzi angapewe bwanji mavuto? Angasonyeze kuti ndi anzeru komanso odziletsa akamapewa malo kapena zochitika zimene zingawapangitse kuti achite zolakwika.