CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Abisalomu Anaukira Chifukwa cha Kunyada
Abisalomu anadzifunira yekha ulemerero (2Sa 15:1; it-1 860)
Abisalomu anakopa mitima ya anthu (2Sa 15:2-6; w12 7/15 13 ¶5)
Abisalomu ankafuna kulanda ufumu wa bambo ake (2Sa 15:10-12; it-1 1083-1084)
Tisalole kuti kulakalaka kwambiri zinthu kuzilamulira mtima wathu. Koma nthawi ndi nthawi tizionanso zimene timalakalaka. M’malo momangofuna kugometsa anthu ena, tiziyesetsa kuganiziranso zofuna zawo.—Afi 2:3, 4.