CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Muzikhala Ndi Mantha Oyenera Poopa Kukhumudwitsa Yehova
Zolinga zabwino sizisintha zimene Mulungu amafuna (2Sa 6:3-5; w05 5/15 17 ¶7)
Uza sanamvere Chilamulo cha Mulungu (2Sa 6:6; w05 2/1 27 ¶20)
Yehova analanga Uza chifukwa choti sanamulemekeze (2Sa 6:7; w05 2/1 27 ¶21)
DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndingasonyeze bwanji kuti ndimaopa kukhumudwitsa Yehova pa moyo wanga?’—Miy 3:7