May 9-15
1 SAMUELI 30-31
Nyimbo Na. 8 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (1 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Dzilimbitseni mwa Yehova Mulungu Wanu”: (10 min.)
Mfundo Zothandiza: (10 min.)
1Sa 30:23, 24—Kodi tikuphunzira chiyani pa nkhani imeneyi? (w05 3/15 24 ¶8)
Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?
Kuwerenga Baibulo: (4 min.) 1Sa 30:1-10 (th phunziro 2)
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Vidiyo ya Ulendo Wobwereza: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo ya Ulendo Wobwereza: Kuvutika—1Yo 5:19. Muziimitsa vidiyoyi nthawi iliyonse imene pali chizindikiro chosonyeza kuti muime n’kufunsa omvera mafunso omwe ali muvidiyoyi.
Ulendo Wobwereza: (3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza. (th phunziro 8)
Ulendo Wobwereza: (5 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza. Mugawireni kabuku kakuti Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, ndipo yambani kuphunzira naye Baibulo mu phunziro 01. (th phunziro 16)
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Khalani Bwenzi la Yehova—Muzipemphera Nthawi Iliyonse: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako ngati n’zotheka, funsani ana omwe munawasankhiratu mafunso awa: N’chifukwa chiyani tiyenera kupemphera kwa Yehova? Kodi ndi pa nthawi ziti pamene tiyenera kupemphera? Kodi ndi zinthu ziti zimene mungatchule m’pemphero?
Zofunika Pampingo: (10 min.)
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lff phunziro 03
Mawu Omaliza (3 min.)
Nyimbo Na. 95 ndi Pemphero