Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

May 22-28

2 MBIRI 25-27

May 22-28

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 136

  • Moyo Wosatha ndi Wabwino Kwambiri Kuposa Zinthu Zimene Tingasiye (Mko 10:29, 30): (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako funsani mafunso otsatirawa: Kodi lonjezo la Yesu lopezeka pa Maliko 10:29, 30, likutilimbikitsa kuchita chiyani? Kodi Yesu anachita chiyani pamene abale ake sanamukhulupirire poyamba? Kodi tiyenera kumakumbukira chiyani zokhudza achibale athu omwe si a Mboni?

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lff phunziro 46

  • Mawu Omaliza (3 min.)

  • Nyimbo Na. 51 ndi Pemphero