Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

June 24-30

MASALIMO 54-56

June 24-30

Nyimbo Na. 48 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Mulungu Ali Kumbali Yanu

(10 min.)

Mukamachita mantha, muzidalira Yehova ngati mmene Davide anachitira (Sl 56:1-4; w06 8/1 22 ¶10-11)

Yehova amayamikira kwambiri mukamapirira ndipo adzakuthandizani (Sl 56:8; cl 243 ¶9)

Yehova ali kumbali yanu. Iye sadzalola kuti chilichonse chikuwonongeni (Sl 56:9-13; Aro 8:36-39; w22.06 18 ¶16-17)

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Sl 55:12, 13​—Kodi Yehova anakonzeratu kuti Yudasi adzapereka Yesu? (it-1 857-858)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(3 min.) KULALIKIRA M’MALO OPEZEKA ANTHU AMBIRI. Muuzeni kuti timaphunzira Baibulo ndi anthu ndipo m’patseni khadi lodziwitsa anthu za phunziroli. (th phunziro 11)

5. Ulendo Wobwereza

(4 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. (lmd phunziro 7 mfundo 4)

6. Nkhani

(5 min.) w23.01 29-30 ¶12-14​—Mutu: Kukonda Khristu Kumatichititsa Kukhala Olimba Mtima. Onani chithunzi. (th phunziro 9)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 153

7. Tikhoza Kumasangalalabe Ngakhale Kuti . . . Tikuopsezedwa ndi Lupanga

(5 min.) Nkhani yokambirana.

Onerani VIDIYO. Kenako funsani omvera funso ili:

  • Kodi mwaphunzira chiyani kuchokera pa zomwe zinachitikira M’bale Dugbe zimene zingakuthandizeni pamene muli ndi mantha?

8. Vidiyo ya Zimene Gulu Lathu Lachita ya June

(10 min.) Onerani VIDIYOYI.

9. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) bt mutu 11 ¶11-19

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 70 ndi Pemphero