June 10-16
MASALIMO 48-50
Nyimbo Na. 126 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)
1. Makolo, Muzithandiza Banja Lanu Kudalira Kwambiri Gulu la Yehova
(10 min.)
Muzithandiza ana anu kuti azikonda kwambiri Yehova komanso gulu lake (Sl 48:12, 13; w22.03 22 ¶11; w11 3/15 19 ¶5-7)
Muziphunzitsa ana anu mbiri ya gulu lathu (w12 8/15 12 ¶5)
Muzikhala chitsanzo pophunzitsa ana anu kutsatira malangizo ochokera ku gulu la Yehova (Sl 48:14)
ZOMWE MUNGACHITE PA KULAMBIRA KWA PABANJA: Nthawi ndi nthawi muzionera ndi kukambirana mavidiyo opezeka pa gawo lakuti “Gulu Lathu” pa jw.org.
2. Mfundo Zothandiza
(10 min.)
-
Sl 49:6, 7—Kodi Aisiraeli ankafunika kumakumbukira chiyani zokhudza chuma chimene anali nacho? (it-2 805)
-
Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
3. Kuwerenga Baibulo
(4 min.) Sl 50:1-23 (th phunziro 11)
4. Kulimba Mtima—Zomwe Yesu Anachita
(7 min.) Nkhani yokambirana. Onerani VIDIYO, kenako kambiranani kabuku ka lmd phunziro 6 mfundo 1-2.
5. Kulimba Mtima—Zomwe Mungachite Potsanzira Yesu
(8 min.) Nkhani yokambirana kuchokera mu kabuku ka lmd phunziro 6 mfundo 3-5 ndi “Onaninso Malemba Awa.”
Nyimbo Na. 73
6. Zofunika Pampingo
(15 min.)
7. Phunziro la Baibulo la Mpingo
(30 min.) bt mutu 11 ¶1-4, mawu ofotokoza gawo 4 ndi bokosi patsamba 86-87