Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

May 13-19

MASALIMO 38-39

May 13-19

Nyimbo Na. 125 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Musamangokhalira Kudziimba Mlandu

(10 min.)

Kudziimba mlandu kwambiri kuli ngati kunyamula katundu wolemera kwambiri (Sl 38:3-8; w20.11 27 ¶12-13)

M’malo momangoganizira zimene munalakwitsa m’mbuyomu, muzikhala wofunitsitsa kuchita zomwe zingasangalatse Yehova (Sl 39:4, 5; w02 11/15 20 ¶1-2)

Ngakhale mukuona kuti n’zovuta kupemphera chifukwa choti mukudziimba mlandu, muzipempherabe (Sl 39:12; w21.10 15 ¶4)

Ngati mukudziimba mlandu kwambiri, muzikumbukira kuti Yehova ‘amakhululukira ndi mtima wonse’ anthu ochimwa omwe alapa.​—Yes 55:7.

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Sl 39:1​—Kodi ndi pa nthawi iti pamene tingagwiritse ntchito mfundo yakuti “ndidzaphimba pakamwa panga kuti ndisalankhule”? (w22.09 13 ¶16)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Kulankhula Mwaluso​—Zomwe Paulo Anachita

(7 min.) Nkhani yokambirana. Onerani VIDIYO, kenako kambiranani kabuku ka lmd phunziro 5 mfundo 1-2.

5. Kulankhula Mwaluso​—Zomwe Mungachite Potsanzira Paulo

(8 min.) Nkhani yokambirana kuchokera mu kabuku ka lmd phunziro 5 mfundo 3-5 ndi “Onaninso Malemba Awa.”

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 44

6. Zofunika Pampingo

(15 min.)

7. Phunziro la Baibulo la Mpingo

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 84 ndi Pemphero