Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

November 14-20

MLALIKI 1-6

November 14-20
  • Nyimbo Na. 66 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Nkhani yokhudza mutu wa pachikuto wa wp16.6—M’patseni munthuyo khadi lodziwitsa anthu za JW.ORG.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Nkhani yokhudza mutu wa pachikuto wa wp16.6—Werengani malemba pogwiritsa ntchito foni kapena tabuleti.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bhs 22-23 ndime 11-12—Muitanireni munthuyo kumisonkhano.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU