November 14-20
MLALIKI 1-6
Nyimbo Na. 66 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Muzisangalala Chifukwa Chogwira Ntchito Mwakhama”: (10 min.)
[Onetsani vidiyo yakuti, Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Mlaliki.]
Mlal. 3:12, 13—Kusangalala ndi ntchito ndi mphatso yochokera kwa Mulungu (w15 2/1 4–6)
Mlal. 4:6—Tiziona moyenera ntchito yathu (w15 2/1 6 ndime 3-5)
Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)
Mlal. 2:10, 11—Kodi Solomo anazindikira mfundo iti yokhudza chuma? (w08 4/15 22 ndime 9-10)
Mlal. 3:16, 17—Kodi tiyenera kuona bwanji zinthu zopanda chilungamo zimene zimachitika m’dzikoli? (w06 11/1 14 ndime 8)
Kodi ndaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kodi ndi mfundo ziti zimene ndaphunzira pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno zimene ndingazigwiritse ntchito mu utumiki?
Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Mlal. 1:1-18
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Nkhani yokhudza mutu wa pachikuto wa wp16.6—M’patseni munthuyo khadi lodziwitsa anthu za JW.ORG.
Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Nkhani yokhudza mutu wa pachikuto wa wp16.6—Werengani malemba pogwiritsa ntchito foni kapena tabuleti.
Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bhs 22-23 ndime 11-12—Muitanireni munthuyo kumisonkhano.
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
“Kodi Tingagwiritse Ntchito Bwanji Buku Lakuti Zimene Baibulo Limaphunzitsa?”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Kenako, onetsani ndiponso kukambirana vidiyo yosonyeza mbali yochepa ya phunziro la Baibulo pogwiritsa ntchito mfundo na. 4 patsamba 115 m’buku lakuti Zimene Baibulo Limaphunzitsa.
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia mutu 11 ndime 1-11
Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)
Nyimbo Na. 112 ndi Pemphero