Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MLALIKI 1-6

Muzisangalala Chifukwa Chogwira Ntchito Mwakhama

Muzisangalala Chifukwa Chogwira Ntchito Mwakhama

Yehova amafuna kuti tizisangalala ndi ntchito yathu ndipo amatiphunzitsa mmene tingachitire zimenezi. Munthu akhoza kumasangalala ndi ntchito yake ngati amaigwira ndi maganizo oyenera.

Mukhoza kumasangalala ndi ntchito yanu . . .

3:13; 4:6

  • mukamaona ntchitoyo moyenera

  • mukamaganizira mmene ntchitoyo imathandizira anthu ena

  • mukamaigwira mwakhama, komabe mukaweruka muziyesetsa kuika maganizo pa banja lanu ndiponso kutumikira Yehova