Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | NYIMBO YA SOLOMO 1-8

Msulami Ndi Chitsanzo Chabwino Kwambiri kwa Atumiki a Yehova

Msulami Ndi Chitsanzo Chabwino Kwambiri kwa Atumiki a Yehova

N’chifukwa chiyani tinganene kuti mtsikanayu ndi chitsanzo chabwino?

2:7; 4:12

  • Anali wanzeru ndipo anadikira mpaka atapeza chikondi chenicheni

  • Sankalola kuti anthu ena amukakamize kuti ayambe chibwenzi ndi munthu wina aliyense

  • Anali wodzichepetsa, wosakonda chuma komanso wodzisunga

  • Sanakopeke ndi zinthu ngati golide kapena mawu okopa achikondi

Dzifunseni kuti:

‘Kodi ndi khalidwe liti la mtsikanayu limene ndiyenera kuyesetsa kumutsanzira?’