Musamakonde Dziko Kapena Zinthu za M’dziko
Satana amagwiritsa ntchito zinthu zitatu zotsatirazi zomwe dziko limalimbikitsa pofuna kutichititsa kuti tisiye kutumikira Yehova. Kodi zinthu zimenezi mungazifotokoze bwanji?
-
“Chilakolako cha thupi”
-
“Chilakolako cha maso”
-
“Kudzionetsera ndi zimene munthu ali nazo”