Zimene Tinganene
●○○ ULENDO WOYAMBA
Funso: Kodi Mulungu anali ndi cholinga chotani potilenga?
Lemba: Gen. 1:27, 28
Funso la Ulendo Wotsatira: N’chifukwa chiyani tiyenera kukhulupirira kuti Mulungu adzakwaniritsa cholinga chake?
○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA
Funso: N’chifukwa chiyani tiyenera kukhulupirira kuti Mulungu adzakwaniritsa cholinga chake?
Lemba: Yos. 21:45
Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi Mulungu watilonjeza chiyani m’tsogolomu?
○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI
Funso: Kodi Mulungu watilonjeza chiyani m’tsogolomu?
Lemba: Chiv. 21:4
Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi tingatani kuti tidzalandire nawo madalitso amene Mulungu walonjeza?