October 1-7
YOHANE 9-10
Nyimbo Na. 25 ndi Pemphero
Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)
CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Yesu Amasamalira Nkhosa Zake”: (10 min.)
Yoh. 10:1-3, 11, 14—Yesu yemwe ndi “m’busa wabwino,” amadziwa nkhosa zake ndipo amazisamalira bwino kwambiri (“Khola la nkhosa” zithunzi ndi mavidiyo pa Yoh. 10:1, nwtsty; w11 5/15 7-8 ¶5)
Yoh. 10:4, 5—Nkhosa zimadziwa mawu a Yesu osati mawu a alendo (cf 125 ¶17)
Yoh. 10:16—Nkhosa za Yesu zimakhala zogwirizana (“kuzibweretsa” mfundo zimene ndikuphunzira pa Yoh. 10:16, nwtsty)
Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)
Yoh. 9:38—Kodi zimene munthu yemwe poyamba anali wakhungu anachita pogwadira Yesu zinkatanthauza chiyani? (“anamugwadira” mfundo zimene ndikuphunzira pa Yoh. 9:38, nwtsty)
Yoh. 10:22—Kodi chikondwerero chopereka kachisi kwa Mulungu chinali chiyani? (“chikondwerero cha kupereka kachisi kwa Mulungu” mfundo zimene ndikuphunzira pa Yoh. 10:22, nwtsty)
Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Yoh. 9:1-17
KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI
Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.
Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba.
Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) fg phunziro 14 ¶1-2
MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Zofunika Pampingo: (15 min.)
Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 7
Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)
Nyimbo Na. 10 ndi Pemphero