“Simuli Mbali ya Dzikoli”
-
Yesu anagonjetsa dziko popewa kuchita zinthu za m’dzikoli
-
Otsatira a Yesu amayenera kuchita zinthu molimba mtima kuti asasokonezeke ndi maganizo komanso zochita za anthu a m’dzikoli
-
Kutengera chitsanzo cha Yesu yemwe anagonjetsa dziko kungatithandize kuti tizichita zinthu molimba mtima