Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

September 12-18

Masalimo 120-134

September 12-18
  • Nyimbo Na. 33 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) wp16.5 tsamba loyamba—Kukambirana ndi mwini nyumba yemwe wakwiya.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) wp16.5 tsamba loyamba—Muitanireni kumisonkhano yathu.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) fg phunziro 8 ndime 6—Thandizani wophunzira wanu kuti azigwiritsa ntchito zimene waphunzira.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 114

  • Yehova Wandichitira Zazikulu: (15 min.) Onerani vidiyo ya pa jw.org. Yehova Wandichitira Zazikulu. (Pitani pamene palembedwa kuti ZOKHUDZA IFEYO > ZIMENE TIMACHITA.) Kenako kambiranani mafunso awa: Kodi Yehova anathandiza bwanji Crystal ndipo zimenezi zamulimbikitsa bwanji? Kodi amachita chiyani akayamba kuganizira zinthu zoipa zimene zinamuchitikira? Kodi mwaphunzira chiyani pa zimene zinachitikira Crystal?

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia mutu 6 ndime 15-23, bokosi patsamba 57 ndi Mfundo Zofunika Kuganizira patsamba 58

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 119 ndi Pemphero