Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MASALIMO 120-134

“Thandizo Langa Lichokera kwa Yehova”

“Thandizo Langa Lichokera kwa Yehova”

Masalimo 120 mpaka 134 amadziwikanso kuti nyimbo zokwerera kumzinda. Anthu ena amakhulupirira kuti Masalimowa ankaimbidwa ndi anthu amene ankapita ku Yerusalemu kukalambira Mulungu. Amakhulupirira kuti anthuwa ankadutsa m’mapiri a ku Yuda akamapita ku zikondwerero za pachaka.

Masalimowa amayerekezera chitetezo cha Yehova ndi . . .

121:3-8

  • M’busa amene ali maso

  • Mthunzi

  • Msilikali wokhulupirika