Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

September 19-25

MASALIMO 135-141

September 19-25
  • Nyimbo Na. 59 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) wp16.5 16

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) wp16.5 16—Muitanireni kumisonkhano yathu

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) fg phunziro 8 ndime 8—Thandizani wophunzira wanu kuti azigwiritsa ntchito zimene waphunzira

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 57

  • Zinthu Zimene Tiyenera Kupewa Tikamachititsa Phunziro la Baibulo”: (15 min.) Mukamaliza kukambirana nkhaniyi, onetsani vidiyo yosonyeza zinthu zoyenera komanso zosayenera kuchita tikamaphunzira Baibulo ndi munthu pogwiritsa ntchito buku la Zimene Baibulo Limaphunzitsa patsamba 31 ndime 7. Limbikitsani ofalitsa onse kuti azitsatira m’mabuku awo pamene vidiyoyi ikuonetsedwa. Pomaliza kumbutsani abale ndi alongo onse omwe amapatsidwa nkhani m’sukulu kuti ngati atamapewa kuchita zinthu zosayenera zomwe takambirana m’nkhaniyi, akhoza kumamaliza nkhani zawo pa nthawi yake.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia mutu 7 ndime 1-14.

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 30 ndi Pemphero