Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MASALIMO 142-150

“Yehova ndi Wamkulu ndi Woyenera Kutamandidwa Kwambiri”

“Yehova ndi Wamkulu ndi Woyenera Kutamandidwa Kwambiri”

145:1-5

Davide anaona kuti ukulu wa Yehova ndi wosasanthulika ndipo zimenezi zinachititsa kuti azitamanda Yehova

145:10-12

Mofanana ndi Davide, atumiki a Yehova okhulupirika amayesetsa kuuza ena ntchito zodabwitsa za Yehova

145:14

Davide ankakhulupirira kuti Yehova amafunitsitsa kuthandiza atumiki ake