Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

October 14-20

MASALIMO 96-99

October 14-20

Nyimbo Na. 66 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. “Muzilengeza Uthenga Wabwino”

(10 min.)

Muziuza ena uthenga wabwino (Sl 96:2; w11 3/1 6 ¶1-2)

Muziwaphunzitsa za uthenga wabwino wonena za Tsiku la Chiweruzo (Sl 96:​12, 13; w12 9/1 16 ¶1)

Muziwathandiza kudziwa cholinga cha Yehova choti padziko lapansi padzaze anthu amene amatamanda dzina lake (Sl 99:​1-3; w12 9/15 12 ¶18-19)

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Sl 96:1—Kodi mawu akuti “nyimbo yatsopano” amanena za chiyani m’malo ambiri amene mawuwa akupezeka? (it-2 994)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Kudzipereka—Zomwe Yesu Anachita

(7 min.) Nkhani yokambirana. Onerani VIDIYO, kenako kambiranani lmd phunziro 10 mfundo 1-2.

5. Kudzipereka—Zomwe Mungachite Potsanzira Yesu

(8 min.) Nkhani yokambirana kuchokera mu kabuku ka lmd phunziro 10 mfundo 3-5 ndi “Onaninso Malemba Awa.”

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 9

6. Zofunika Pampingo

(15 min.)

7. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) bt mutu 16 ¶10-18

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 67 ndi Pemphero