Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

October 21-27

MASALIMO 100-102

October 21-27

Nyimbo Na. 37 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Muziyamikira Chikondi Chokhulupirika cha Yehova

(10 min.)

Muzikonda kwambiri Yehova (Sl 100:5; w23.03 12 ¶18-19)

Muzipewa zinthu zimene zingawononge ubwenzi wanu ndi Yehova (Sl 101:​2, 3; w23.02 17 ¶10)

Muzipewa anthu amene amanena zabodza zokhudza Yehova ndi gulu lake (Sl 101:5; w11 7/15 16 ¶7-8)

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndikhoza kuwononga ubwenzi wanga ndi Yehova chifukwa cha mmene ndimagwiritsira ntchito intaneti?’

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Sl 102:6—N’chifukwa chiyani wolemba salimoli anadziyerekezera ndi mbalame yotchedwa vuwo? (it-2 596)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(3 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. (lmd phunziro 2 mfundo 3)

5. Ulendo Wobwereza

(5 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. M’pempheni kuti muziphunzira naye Baibulo. (lmd phunziro 9 mfundo 4)

6. Kufotokoza Zimene Mumakhulupirira

(4 min.) Chitsanzo. ijwbq 129—Mutu: Kodi Baibulo Linasinthidwa Kapena Kusokonezedwa? (th phunziro 8)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 137

7. ‘Ndikumamatirani, Inuyo Mundigwire Mwamphamvu’

(15 min.)

Nkhani yokambirana. Onerani VIDIYO. Kenako funsani mafunso awa:

  • Kodi Anna anasonyeza bwanji chikondi chokhulupirika?

  • Kodi tingamutsanzire bwanji?

8. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) bt mutu 17 ¶1-7

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 96 ndi Pemphero