Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

September 9-15

MASALIMO 82-84

September 9-15

Nyimbo Na. 80 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Mmodzi wa ana a Kora akuyang’ana mosirira chisa cha namzeze chomwe chili m’bwalo la kachisi

1. Tiziyamikira Mwayi wa Utumiki Umene Tili Nawo

(10 min.)

Timayamikira mwayi wa utumiki umene tili nawo (Sl 84:​1-3; wp16.6 8 ¶2-3)

Tizisangalala ndi utumiki umene tikuchita panopa, m’malo momaganizira kwambiri za utumiki umene timalakalaka (Sl 84:10; w08 7/15 30 ¶3-4)

Yehova ndi wabwino kwa anthu amene amamutumikira mokhulupirika (Sl 84:11; w20.01 17 ¶12)

Utumiki uliwonse umakhala ndi madalitso ake komanso mavuto ake. Tikamaganizira madalitso amene timapeza, tikhoza kumasangalala ndi utumiki uliwonse.

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Sl 82:3—Kodi kusonyeza chikondi “ana amasiye” mumpingo n’kofunika bwanji? (it-1 816)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Kukhala Achifundo—Zomwe Yesu Anachita

(7 min.) Nkhani yokambirana. Onerani VIDIYO, kenako kambiranani kabuku ka lmd phunziro 9 mfundo 1-2.

5. Kukhala Achifundo—Zomwe Mungachite Potsanzira Yesu

(8 min.) Nkhani yokambirana kuchokera m’kabuku ka lmd phunziro 9 mfundo 3-5 ndi “Onaninso Malemba Awa.”

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 57

6. Zofunika Pampingo

(15 min.)

7. Phunziro la Baibulo la Mpingo

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 130 ndi Pemphero