September 9-15
MASALIMO 82-84
Nyimbo Na. 80 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)
1. Tiziyamikira Mwayi wa Utumiki Umene Tili Nawo
(10 min.)
Timayamikira mwayi wa utumiki umene tili nawo (Sl 84:1-3; wp16.6 8 ¶2-3)
Tizisangalala ndi utumiki umene tikuchita panopa, m’malo momaganizira kwambiri za utumiki umene timalakalaka (Sl 84:10; w08 7/15 30 ¶3-4)
Yehova ndi wabwino kwa anthu amene amamutumikira mokhulupirika (Sl 84:11; w20.01 17 ¶12)
Utumiki uliwonse umakhala ndi madalitso ake komanso mavuto ake. Tikamaganizira madalitso amene timapeza, tikhoza kumasangalala ndi utumiki uliwonse.
2. Mfundo Zothandiza
(10 min.)
Sl 82:3—Kodi kusonyeza chikondi “ana amasiye” mumpingo n’kofunika bwanji? (it-1 816)
Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
3. Kuwerenga Baibulo
(4 min.) Sl 82:1–83:18 (th phunziro 2)
4. Kukhala Achifundo—Zomwe Yesu Anachita
(7 min.) Nkhani yokambirana. Onerani VIDIYO, kenako kambiranani kabuku ka lmd phunziro 9 mfundo 1-2.
5. Kukhala Achifundo—Zomwe Mungachite Potsanzira Yesu
(8 min.) Nkhani yokambirana kuchokera m’kabuku ka lmd phunziro 9 mfundo 3-5 ndi “Onaninso Malemba Awa.”
Nyimbo Na. 57
6. Zofunika Pampingo
(15 min.)
7. Phunziro la Baibulo la Mpingo
(30 min.) bt mutu 15 ¶8-12, bokosi patsamba 118