Banja la Yehova Logwirizana
M’mawa
-
9:30 Kumvetsera Nyimbo
-
9:40 Nyimbo Na. 85 ndi Pemphero
-
9:50 Muziyamikira Mwayi Wanu Wokhala M’banja la Yehova
-
10:05 Nkhani Yosiyirana: Anathandiza Kuti Ena Azimva Bwino
-
• Elihu
-
• Lidiya
-
• Yesu
-
-
11:05 Nyimbo Na. 100 ndi Zilengezo
-
11:15 Pitirizani Kuthandiza Ena Kuti Akhale M’banja la Yehova
-
11:30 Kudzipereka Ndiponso Kubatizidwa
-
12:00 Nyimbo Na. 135
Masana
-
1:10 Kumvetsera Nyimbo
-
1:20 Nyimbo Na. 132 ndi Pemphero
-
1:30 Nkhani ya Baibulo ya Onse: Kodi Panyumba Panu Ndi Malo a Mpumulo Ndi Mtendere?
-
2:00 Phunziro Lachidule la Nsanja ya Olonda
-
2:30 Nyimbo Na. 136 ndi Zilengezo
-
2:40 Nkhani Yosiyirana: Muzilimbikitsa Mtendere
-
• Muzilankhula ‘Mawu Olimbikitsa’
-
• ‘Muziyenda M’chikondi’
-
• Muzipewa Adani Athu
-
-
3:40 ‘Tisamaleke Kuyamika Mulungu’ Chifukwa cha Abale ndi Alongo Athu
-
4:15 Nyimbo Na. 107 ndi Pemphero