Mupeze Mayankho a Mafunso Awa
1. Kodi tingasonyeze bwanji kuti timayamikira malo omwe tili nawo m’banja la Yehova? (Aef. 4:3)
2. Kodi tingatani kuti tizichititsa ena kuti azimva bwino, nanga tingachite bwanji zimenezi? (Aroma 15:7)
3. Kodi tingatani kuti tithandize anthu ambiri kuti abwere m’banja la Yehova? (Aef. 2:17; 6:15)
4. Kodi tingatani kuti tikhale anthu olimbikitsa mtendere? (Aef. 4:29; 5:1, 2; 6:13)
5. Kodi tingatani kuti tizikonda kwambiri abale ndi alongo athu? (Aef. 1:15, 16)
© 2022 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
CA-copgm23-CN