Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Nkhani Zokhudza Ndalama

Nkhani Zokhudza Ndalama

Chigawo 5

Nkhani Zokhudza Ndalama

Kodi mumaona kuti ndalama n’zofunika kuti mukhale wosangalala?

□ N’zosafunika

□ N’zofunika pang’ono

□ N’zofunika kwambiri

Kodi mumakonda kulankhula za ndalama ndiponso zinthu zimene mungagule?

□ Ayi

□ Nthawi zina

□ Nthawi zambiri

N’kutheka kuti makolo anu akuuzanipo mobwerezabwereza kuti ndalama zimafunika kukhetsera thukuta. Zimenezo n’zoona, ndipo n’chifukwa chake muyenera kuzigwiritsa ntchito mosamala. Ngakhale kuti ndalama n’zofunika, zikhoza kukusokonezani maganizo, kukudanitsani ndi anthu ena, ndiponso zingawonongetse ubwenzi wanu ndi Mulungu. Ndipotu moyo wanu ungakhudzidwe kwambiri ndi mmene mumaonera ndalama. Werengani Mitu 18 mpaka 20 kuti muziona ndalama m’njira yoyenera.

[Chithunzi chachikulu pamasamba 148, 149]