Mupeze Mayankho a Mafunso Awa
1. Kodi tingalowe bwanji mu mpumulo wa Mulungu? (Gen. 2:1-3; Aheb. 4:1, 11)
2. Kodi tingatani kuti mphamvu ya “mawu a Mulungu” isinthe moyo wathu? (1 Ates. 2:13; Aheb. 4:12)
3. N’chifukwa chiyani tiyenera kudalira Yehova kuti azititsogolera? (Yes. 26:7-9, 15, 20)
4. Kodi tiyenera kuchita zotani kuti Yehova atidalitse? (1 Pet. 1:13-15; 1 Yoh. 5:3)
5. Kodi tingatani kuti tizisangalatsa mtima wa Yehova? (Sal. 71:14, 15; Aroma 12:2; 1 Pet. 4:10)
6. Mungatani kuti muzisangalala potumikira Yehova? (Yoh. 5:17)
© 2023 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
CA-brpgm24-CN